Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Ahebri 10:18 - Buku Lopatulika

Koma pomwe pali chikhululukiro cha machimo palibenso chopereka cha kwa uchimo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma pomwe pali chikhululukiro cha machimo palibenso chopereka cha kwa uchimo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamene Mulungu wakhululukira zonsezi, sipafunikanso nsembe yoperekera machimo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndipo pamene machimo akhululukidwa, sipafunikanso nsembe yoperekedwa chifukwa cha machimowo.

Onani mutuwo



Ahebri 10:18
4 Mawu Ofanana  

Pakuti ndi chipereko chimodzi anawayesera angwiro chikhalire iwo oyeretsedwa.


ndipo machimo ao ndi kusaweruzika kwao sindidzakumbukiranso.


Ndipo pokhala nacho, abale, chilimbikitso chakulowa m'malo opatulika, ndi mwazi wa Yesu,


Pakadapanda kutero, kodi sakadaleka kuzipereka, chifukwa otumikirawo sakadakhala nacho chikumbumtima cha machimo, popeza adayeretsedwa kamodzi?