Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Ahebri 10:13 - Buku Lopatulika

kuyambira pomwepo alindirira, kufikira adani ake aikidwa akhale mpando kumapazi ake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

kuyambira pomwepo alindirira, kufikira adani ake aikidwa akhale mpando kumapazi ake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kumeneko akudikira tsono kuti Mulungu asandutse adani ake kukhala ngati chopondapo mapazi ake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kumeneko akudikira tsono kuti Mulungu asandutse adani ake kukhala chopondapo mapazi ake.

Onani mutuwo



Ahebri 10:13
8 Mawu Ofanana  

Yehova ananena kwa Ambuye wanga, Khalani padzanja lamanja langa, kufikira nditaika adani anu chopondapo mapazi anu.


Ndipo masiku a mafumu aja Mulungu wa Kumwamba adzaika ufumu woti sudzaonongeka kunthawi zonse, ndi ulamuliro wake sudzasiyidwira mtundu wina wa anthu, koma udzaphwanya ndi kutha maufumu ao onse, nudzakhala chikhalire.


Ambuye ananena kwa Ambuye wanga, ukhale padzanja lamanja langa, kufikira Ine ndidzaika adani ako pansi pa mapazi ako.


Davide mwini yekha anati mwa Mzimu Woyera, Ambuye anati kwa Ambuye wanga, Khala kudzanja langa lamanja, kufikira ndiwaika adani ako popondapo mapazi ako.


kufikira Ine ndikaika adani ako pansi pa mapazi ako.


kufikira ndikaike adani ako chopondapo mapazi ako.


Pakuti ayenera kuchita ufumu kufikira ataika adani onse pansi pa mapazi ake.


Koma za mngelo uti anati nthawi iliyonse, Khala padzanja lamanja langa, Kufikira ndikaika adani ako mpando wa kumapazi ako?