Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




Aefeso 6:7 - Buku Lopatulika

akuchita ukapolo ndi kuvomereza mtima, monga kutumikira Ambuye Yesu Khristu, si anthu ai;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

akuchita ukapolo ndi kuvomereza mtima, monga kutumikira Ambuye Yesu Khristu, si anthu ai;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Muzitumikira mosangalala, ngati kuti mukutumikira Ambuye, osati anthu chabe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tumikirani ndi mtima wonse, ngati kuti mukutumikira Ambuye, osati anthu.

Onani mutuwo



Aefeso 6:7
8 Mawu Ofanana  

Ndipo inu mudziwa kuti ndi mphamvu zanga zonse ndatumikira atate wanu.


Pamenepo anyamata ake anasendera, nanena naye, nati, Atate wanga, mneneri akadakuuzani chinthu chachikulu, simukadachichita kodi? Koposa kotani nanga ponena iye, Samba, nukonzeke?


Koma ayamikidwe Mulungu, kuti ngakhale mudakhala akapolo a uchimo, tsopano mwamvera ndi mtima makhalidwe aja a chiphunzitso chimene munaperekedweracho;


Chifukwa chake mungakhale mudya, mungakhale mumwa, mungakhale muchita kanthu kena, chitani zonse ku ulemerero wa Mulungu.


chilichonse mukachichita, gwirani ntchito mochokera mumtima, monga kwa Ambuye, osati kwa anthu ai;