Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




3 Yohane 1:13 - Buku Lopatulika

Ndinali nazo zambiri za kukulembera, komatu sindifuna kukulembera ndi kapezi ndi peni;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndinali nazo zambiri za kukulembera, komatu sindifuna kukulembera ndi kapezi ndi peni;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndinali ndi zambiri zoti ndikuuze, koma sindingakonde kuzilemba m'kalata.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ndili ndi zambiri zoti ndikulembereni, koma sindikufuna kuzilemba mʼkalata.

Onani mutuwo



3 Yohane 1:13
2 Mawu Ofanana  

Koma Yosefe, mwamuna wake, anali wolungama, ndiponso sanafune kunyazitsa iye, nayesa m'mtima kumleka iye m'tseri.


Pokhala ndili nazo zambiri zakukulemberani, sindifuna kuchita ndi kalata ndi kapezi; koma ndiyembekeza kudza kwa inu, ndi kulankhula popenyana, kuti chimwemwe chanu chikwanire.