Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Yohane 1:13 - Buku Lopatulika

Akupereka moni ana a mbale wanu wosankhika.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Akupereka moni ana a mbale wanu wosankhika.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ana a mbale wanu wosankhidwa ndi Mulungu akuti moni.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ana a mlongo wanu wosankhidwa ndi Mulungu akupereka moni.

Onani mutuwo



2 Yohane 1:13
3 Mawu Ofanana  

Ndipo ngati mupatsa moni abale anu okhaokha, muchitanji choposa ena? Kodi angakhale anthu akunja sachita chomwecho?


Iye wa ku Babiloni wosankhidwa pamodzi nanu akukupatsani moni; ateronso Marko mwana wanga.