Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Yohane 1:11 - Buku Lopatulika

Pakuti iye wakumpatsa moni ayanjana nazo ntchito zake zoipa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti iye wakumpatsa moni ayanjana nazo ntchito zake zoipa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

pakuti wopatsa munthu wotere moni, akuvomereza zochita zake zoipa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Aliyense wolandira munthu wotere ndiye kuti akuvomerezana nazo ntchito zake zoyipa.

Onani mutuwo



2 Yohane 1:11
6 Mawu Ofanana  

Pakuona mbala, uvomerezana nayo, nuchita nao achigololo.


ndipo musayanjane nazo ntchito za mdima zosabala kanthu, koma makamakanso muzitsutse;


Usafulumira kuika manja pa munthu aliyense, kapena usayanjana nazo zoipa za eni; udzisunge wekha woyera mtima.


Pakuti yense wakudya mkaka alibe chizolowezi cha mau a chilungamo; pakuti ali khanda.


koma ena muwapulumutse ndi kuwakwatula kumoto; koma ena muwachitire chifundo ndi mantha, nimudane naonso malaya ochitidwa mawanga ndi thupi.


Ndipo ndinamva mau ena ochokera Kumwamba, nanena, Tulukani m'menemo, anthu anga; kuti mungayanjane ndi machimo ake, ndi kuti mungalandireko ya miliri yake;