Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Timoteyo 4:9 - Buku Lopatulika

Tayesetsa kudza kwa ine msanga:

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Tayesetsa kudza kwa ine msanga:

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Uyesetse kubwera kuno msanga.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Uyesetse kubwera kuno msanga.

Onani mutuwo



2 Timoteyo 4:9
4 Mawu Ofanana  

Pakuti pamene ulikupita naye mnzako wa mlandu kwa oweruza, fulumira panjira kutha naye mlandu, kuti angakokere iwe kwa oweruza, ndipo oweruzayo angapereke iwe kwa msilikali, ndi msilikali angaponye iwe m'nyumba yandende.


pokhumba usiku ndi usana kukuona iwe, ndi kukumbukira misozi yako, kuti ndidzazidwe nacho chimwemwe;


Tayesetsa kudza isanadze nyengo yachisanu. Akukupatsa moni Yubulo, ndi Pude, ndi Lino, ndi Klaudia, ndi abale onse.


Pamene ndikatuma Aritema kwa iwe, kapena Tikiko, chita changu kudza kwa ine ku Nikopoli: pakuti ndatsimikiza mtima kugonerako nyengo yachisanu.