Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 23:39 - Buku Lopatulika

Uriya Muhiti; onse pamodzi anali makumi atatu mphambu asanu ndi awiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Uriya Muhiti; onse pamodzi anali makumi atatu mphambu asanu ndi awiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Uriya Muhiti uja. Onse pamodzi anali anthu 37.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

ndi Uriya Mhiti. Onse pamodzi analipo 37.

Onani mutuwo



2 Samueli 23:39
7 Mawu Ofanana  

Ndipo Davide anatumiza munthu nafunsa za mkaziyo. Ndipo wina anati, Sindiye Bateseba, mwana wamkazi wa Eliyamu, mkazi wa Uriya Muhiti?


Chifukwa ninji unapeputsa mau a Yehova ndi kuchita chimene chili choipa pamaso pake? Unakantha Uriya Muhiti ndi lupanga ndi kutenga mkazi wake akhale mkazi wako; ndipo unamupha iye ndi lupanga la ana a Amoni.


chifukwa kuti Davide adachita cholungama pamaso pa Yehova, osapatuka masiku ake onse pa zinthu zonse adamlamulira Iye, koma chokhacho chija cha Uriya Muhiti.


Uriya Muhiti, Zabadi mwana wa Alai,


ndi Yese anabala Davide mfumuyo. Ndipo Davide anabala Solomoni mwa mkazi wa Uriya;


Pamenepo Davide anayankha nati kwa Ahimeleki Muhiti, ndi Abisai, mwana wa Zeruya, mbale wake wa Yowabu, nati, Adzatsikira nane ndani kumisasako kwa Saulo? Nati Abisai, Nditsika nanu ndine.