Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 23:37 - Buku Lopatulika

Zeleki Mwamoni, Naharai Mbeeroti, onyamula zida za Yowabu mwana wa Zeruya;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Zeleki Mwamoni, Naharai Mbeeroti, onyamula zida za Yowabu mwana wa Zeruya;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Zeleki Mwamoni, Naharai wa ku Beeroti, wonyamula zida za Yowabu, mwana wa Zeruya,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Zeleki Mwamoni, Naharai wa ku Beeroti, mnyamata wonyamula zida za Yowabu mwana wa Zeruya,

Onani mutuwo



2 Samueli 23:37
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Isiboseti, mwana wa Saulo anali nao amuna awiri, ndiwo atsogoleri a magulu; wina dzina lake Baana, ndi dzina la mnzake ndiye Rekabu, ndiwo ana a Rimoni wa ku Beeroti, wa ana a Benjamini, pakuti Beeroti womwe unawerengedwa wa Benjamini;


Heziro wa ku Karimele, Naarai mwana wa Ezibai,


Zeleki Mwamoni, Naharai Mbeeroti wonyamula zida za Yowabu mwana wa Zeruya,


Pamenepo anaitana msanga mnyamata wake wosenza zida zake, nanena naye, Solola lupanga lako nundiphe, angamanenere anthu, ndi kuti, Anamupha ndi mkazi. Nampyoza mnyamata wake, nafa iye.