Ndipo wotsatana naye ndiye Sama mwana wa Age Muharari. Ndipo Afilisti anasonkhana ali gulu pa Lehi pamene panali munda wamphodza; anthu nathawa Afilistiwo.
2 Samueli 23:33 - Buku Lopatulika Sama Muharari, Ahiyamu mwana wa Sarara Muharari; Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Sama Muharari, Ahiyamu mwana wa Sarara Muharari; Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa Sama Muharari, Ahiyamu mwana wa Sarara Muharari, Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero mwana wa Sama Mharari, Ahiamu mwana wa Sarari Mharari, |
Ndipo wotsatana naye ndiye Sama mwana wa Age Muharari. Ndipo Afilisti anasonkhana ali gulu pa Lehi pamene panali munda wamphodza; anthu nathawa Afilistiwo.