Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 23:28 - Buku Lopatulika

Zalimoni Mwahohi, Maharai Mnetofa;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Zalimoni Mwahohi, Maharai Mnetofa;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Zalimoni Mwahohi, Maharai wa ku Netofa,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Zalimoni Mwahohi, Maharai Mnetofa,

Onani mutuwo



2 Samueli 23:28
7 Mawu Ofanana  

Ndipo pamene anamva akazembe onse a makamu, iwo ndi anthu ao, kuti mfumu ya Babiloni adaika Gedaliya wowalamulira, anadza kwa Gedaliya ku Mizipa, ndiwo Ismaele mwana wa Netaniya, ndi Yohanani mwana wa Kareya, ndi Seraya mwana wa Tanumeti wa ku Netofa, ndi Yazaniya mwana wa Mmaakati, iwo ndi anthu ao omwe.


Maharai Mnetofa, Heledi mwana wa Baana Mnetofa,


Wakhumi wa mwezi wakhumi ndiye Maharai Mnetofa wa Azera; ndi m'chigawo mwake zikwi makumi awiri mphambu zinai.


ndi Abisuwa, ndi Naamani, ndi Ahowa,


Anthu a ku Netofa, makumi asanu mphambu asanu ndi mmodzi.


Amuna a ku Betelehemu ndi ku Netofa, zana limodzi mphambu makumi asanu ndi atatu kudza asanu ndi atatu.


pamenepo anadza kwa Gedaliya ku Mizipa, Ismaele mwana wa Netaniya, ndi Yohanani ndi Yonatani ana a Kareya, ndi Seraya mwana wa Tanumeti, ndi ana a Efayi wa ku Netofa, ndi Yezaniya mwana wa munthu wa ku Maaka, iwo ndi anthu ao.