Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 23:27 - Buku Lopatulika

Abiyezere Mwanatoti, Mebunai Muhusa;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Abiyezere Mwanatoti, Mebunai Muhusa;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Abiyezere wa ku Anatoti, Mebunai Muhusa,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Abiezeri wa ku Anatoti, Sibekai Mhusati,

Onani mutuwo



2 Samueli 23:27
5 Mawu Ofanana  

Ndipo kunali chitapita ichi, kunalinso nkhondo ndi Afilisti ku Gobu; pamenepo Sibekai Muhusa anapha Safi, ndiye wa ana a Rafa.


nati, Pali Mulungu wanga, kukhale kutali kwa ine kuchita ichi. Ngati ndidzamwa mwazi wa anthu awa? Akadataya moyo wao, inde akadataya moyo wao, pakukatenga madziwa. M'mwemo sanafune kuwamwa. Izi anazichita atatu amphamvuwa.


Ira mwana wa Ikesi wa ku Tekowa, Abiyezere wa ku Anatoti,


Wachisanu ndi chinai wa mwezi wachisanu ndi chinai ndiye Abiyezere Mwanatoti wa Abenjamini; ndi m'chigawo mwake zikwi makumi awiri mphambu zinai.


Anatoti ndi mabusa ake, ndi Alimoni ndi mabusa ake; mizinda inai.