Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 23:13 - Buku Lopatulika

Ndipo atatu a mwa makamu atatu opambanawo, anatsika nafika kwa Davide nyengo ya kukolola m'phanga la ku Adulamu; ndi gulu la Afilisti linamanga zithando m'chigwa cha Refaimu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo atatu a mwa makamu atatu opambanawo, anatsika nafika kwa Davide nyengo ya kukolola m'phanga la ku Adulamu; ndi gulu la Afilisti linamanga zithando m'chigwa cha Refaimu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nthaŵi yokolola, atatu mwa ankhondo otchuka makumi atatu aja, adapita kwa Davide ku phanga la Adulamu, pamene gulu lankhondo la Afilisti linkamanga zithando zankhondo ku chigwa cha Refaimu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pa nthawi yokolola, atatu mwa atsogoleri makumi atatu anabwera kwa Davide ku phanga la Adulamu, pamene gulu la Afilisti linali litamanga misasa mʼchigwa cha Refaimu.

Onani mutuwo



2 Samueli 23:13
9 Mawu Ofanana  

Tsono Afilisti anafika natanda m'chigwa cha Refaimu.


Ndipo Afilisti anakweranso kachiwiri, natanda m'chigwa cha Refaimu.


Afilisti tsono anafika, nafalikira m'chigwa cha Refaimu.


Ndipo padzakhala ngati wamasika alikumweta tirigu wosacheka, ndi dzanja lake lilikudula ngala; inde padzakhala ngati pamene wina akunkha ngala m'chigwa cha Refaimu.


Ndidzakutengeranso wokhala mu Maresa iwe, iye amene adzakulandira ukhale cholowa chake; ulemerero wa Israele udzafikira ku Adulamu.


mfumu ya ku Libina, imodzi; mfumu ya ku Adulamu, imodzi;


Yaramuti, ndi Adulamu, Soko, ndi Azeka;


Motero Davide anachoka kumeneko, napulumukira ku phanga la ku Adulamu; ndipo pamene abale ake ndi banja lonse la atate wake anamva, iwo anatsikira kumeneko kwa iye.