Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 22:37 - Buku Lopatulika

Munakulitsa kulunza kwanga pansi panga, ndi mapazi anga sanaterereke.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Munakulitsa kulunza kwanga pansi panga, ndi mapazi anga sanaterereke.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Mwalimbitsa miyendo yanga kuti ndiyende bwino, choncho mapazi anga sadaterereke.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Inu mwalimbitsa njira yanga kuti ndiyende bwino, kuti mapazi anga asaterereke.

Onani mutuwo



2 Samueli 22:37
8 Mawu Ofanana  

Iye ananditulutsanso ku malo aakulu; Iye anandipulumutsa, chifukwa akondwera ndi ine.


Sadzalola phazi lako literereke: Iye amene akusunga sadzaodzera.


M'mayendedwe anga ndasunga mabande anu, mapazi anga sanaterereke.


Mwandipondetsa patalipatali, sanaterereke mapazi anga.


Pakufuula ine mundiyankhe, Mulungu wa chilungamo changa; pondichepera mwandikulitsira malo. Ndichitireni chifundo, imvani pemphero langa.


Pamene ndinati, Literereka phazi langa, chifundo chanu, Yehova, chinandichirikiza.


Mapazi ako sadzaombana ulikuyenda; ukathamanga, sudzaphunthwa.


Adzasunga mapazi a okondedwa ake, koma oipawo adzawakhalitsa chete mumdima; pakuti palibe munthu adzapambana ndi mphamvu.