Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 22:35 - Buku Lopatulika

Iye aphunzitsa manja anga nkhondo; kotero kuti manja anga alifula uta wamkuwa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Iye aphunzitsa manja anga nkhondo; kotero kuti manja anga alifula uta wamkuwa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Amaphunzitsa manja anga kamenyedwe ka nkhondo, kotero kuti ndingathe kupinda uta wachitsulo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iye amaphunzitsa manja anga kuchita nkhondo; manja anga amatha kuthyola uta wachitsulo.

Onani mutuwo



2 Samueli 22:35
7 Mawu Ofanana  

Adzathawa chida chachitsulo, ndi muvi wa uta wamkuwa udzampyoza.


Wolemekezeka Yehova thanthwe langa, wakuphunzitsa manja anga achite nkhondo, zala zanga zigwirane nao:


Aletsa nkhondo ku malekezero a dziko lapansi; athyola uta, nadula nthungo; atentha magaleta ndi moto.


ndipo ndidzakantha uta wako kuuchotsa m'dzanja lako lamanzere, ndi kutayitsa mivi yako kudzanja lako lamanja.


Ndipo Davide anati kwa Mfilistiyo, Iwe ukudza kwa ine ndi lupanga, ndi mkondo, ndi nthungo; koma ine ndafika kwa iwe m'dzina la Yehova wa makamu, Mulungu wa ankhondo a Israele amene iwe unawanyoza.