Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Samueli 20:25 - Buku Lopatulika

ndi Seva anali mlembi; ndi Zadoki ndi Abiyatara anali ansembe;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi Seva anali mlembi; ndi Zadoki ndi Abiyatara anali ansembe;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Seva anali mlembi wa mfumu. Zadoki ndi Abiyatara anali ansembe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Seva anali mlembi wa mfumu. Zadoki ndi Abiatara anali ansembe

Onani mutuwo



2 Samueli 20:25
7 Mawu Ofanana  

Ndipo onani, Zadoki yemwe anadza, ndi Alevi onse pamodzi naye, alikunyamula likasa la chipangano la Mulungu; natula likasa la Mulungu; ndi Abiyatara anakwera kufikira anthu onse anatha kutuluka m'mzindamo.


ndiponso Ira Myairi anali ansembe a Davide.


ndi Zadoki mwana wa Ahitubi, ndi Ahimeleki mwana wa Abiyatara anali ansembe, ndi Seraya anali mlembi.


Ndipo anapangana ndi Yowabu mwana wa Zeruya, ndi Abiyatara wansembeyo; ndipo amenewo anamtsata Adoniya namthandiza.


Koma Zadoki wansembe, ndi Benaya mwana wake wa Yehoyada, ndi Natani mneneri, ndi Simei, ndi Rei, ndi anthu amphamvu aja adaali ndi Davide, sanali ndi Adoniya.


ndi Benaya mwana wa Yehoyada anali kazembe wa nkhondo, ndi Zadoki ndi Abiyatara anali ansembe,


Ndi Zadoki mwana wa Ahitubi, ndi Ahimeleki mwana wa Abiyatara, anali ansembe, ndi Savisa anali mlembi,