Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Mafumu 4:3 - Buku Lopatulika

Pamenepo anati, Kabwereke zotengera kwina kwa anansi ako onse, zotengera zopanda kanthu, zisakhale pang'ono.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo anati, Kabwereke zotengera kwina kwa anansi ako onse, zotengera zopanda kanthu, zisakhale pang'ono.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo Elisayo adamuuza kuti, “Pitani, kabwerekeni mitsuko yambirimbiri kwa anzanu.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Elisa anati, “Pita kabwereke mitsuko yonse yopanda kanthu kwa anzako. Usakabwereke mitsuko yochepa.

Onani mutuwo



2 Mafumu 4:3
8 Mawu Ofanana  

Ndipo anati, Atero Yehova, Kumbani m'chigwa muno mukhale maenje okhaokha.


Ndipo Elisa anati kwa iye, Ndikuchitire chiyani? Undiuze m'nyumba mwako muli chiyani? Nati, Mdzakazi wanu alibe kanthu m'nyumba, koma mtsuko wa mafuta.


Nulowe, nudzitsekere wekha ndi ana ako aamuna ndi kutsanulira m'zotengera zonsezi, nuike padera zodzalazo.


Ine ndine Yehova Mulungu wako amene ndinakukweza kukuchotsa kudziko la Ejipito; yasamitsa pakamwa pako ndipo ndidzalidzaza.


Koma anthu anga sanamvere mau anga; ndipo Israele sanandivomere.


Kufikira tsopano simunapemphe kanthu m'dzina langa; pemphani, ndipo mudzalandira, kuti chimwemwe chanu chikwaniridwe.


Yesu ananena nao, Dzazani mitsukoyo ndi madzi. Naidzaza, ndendende.