Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Mafumu 3:5 - Buku Lopatulika

Koma kunachitika, atafa Ahabu mfumu ya Mowabu anapandukana ndi mfumu ya Israele.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma kunachitika, atafa Ahabu mfumu ya Mowabu anapandukana ndi mfumu ya Israele.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma Ahabu atamwalira, mfumu ya Amowabuyo idagalukira mfumu ya ku Israele.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma atamwalira Ahabu, mfumu ya ku Mowabu inawukira mfumu ya ku Israeli.

Onani mutuwo



2 Mafumu 3:5
5 Mawu Ofanana  

Ndipo atamwalira Ahabu, Mowabu anapandukana ndi Israele.


Pamenepo Elisa anamwalira, ndipo anamuika. Ndipo magulu a Amowabu analowa m'dziko poyambira chaka.


Ndipo mfumu Yehoramu anatuluka mu Samariya nthawi yomweyo, namemeza Aisraele onse.


Masiku ake Aedomu anapanduka ku ulamuliro wa Yuda, nadziikira mfumu okha.