Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Mafumu 15:3 - Buku Lopatulika

Nachita iye zoongoka pamaso pa Yehova, monga mwa zonse adazichita atate wake Amaziya.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Nachita iye zoongoka pamaso pa Yehova, monga mwa zonse adazichita atate wake Amaziya.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Azariya adachita zolungama pamaso pa Chauta, monga momwe ankachitira bambo wake Amaziya.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Iyeyo anachita zabwino pamaso pa Yehova, monga momwe anachitira Amaziya abambo ake.

Onani mutuwo



2 Mafumu 15:3
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Asa anachita zabwino pamaso pa Yehova monga Davide kholo lake.


Anali wa zaka khumi ndi zisanu ndi chimodzi polowa ufumu wake, nakhala mfumu zaka makumi asanu mphambu ziwiri mu Yerusalemu; ndi dzina la make ndiye Yekoliya wa ku Yerusalemu.


Nachita iye zoongoka pamaso pa Yehova; anachita monga mwa zonse anazichita atate wake Uziya.


Komatu sanaichotse misanje; anthu anapherabe nsembe, nafukiza pamisanje.


Uziya anali wa zaka khumi mphambu zisanu ndi chimodzi polowa ufumu wake, nakhala mfumu mu Yerusalemu zaka makumi asanu mphambu ziwiri; ndi dzina la make ndiye Yekoliya wa ku Yerusalemu.


Nachita iye zoongoka pamaso pa Yehova, monga mwa zonse adazichita atate wake Amaziya.