Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Akorinto 3:15 - Buku Lopatulika

Koma kufikira lero, pamene awerengedwa Mose, chophimba chigona pamtima pao.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma kufikira lero, pamene awerengedwa Mose, chophimba chigona pamtima pao.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndithu, mpaka lero lino nthaŵi zonse akamaŵerenga Malamulo a Mose, chophimba chija chimaphimbabe mitima yao.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ngakhale lero lomwe lino akuwerenga mabuku a Mose pali chophimbabe mitima yawo.

Onani mutuwo



2 Akorinto 3:15
4 Mawu Ofanana  

Ndipo Iye adzaononga m'phiri limeneli chophimba nkhope chovundikira mitundu yonse ya anthu, ndi nsalu yokuta amitundu onse.


koma mitima yao inaumitsidwa; pakuti kufikira lero lomwe lino, pa kuwerenga kwa pangano lakale chophimba chomwechi chikhalabe chosavundukuka, chimene chilikuchotsedwa mwa Khristu.


Koma pamene akatembenukira kwa Ambuye, chophimbacho chichotsedwa.