Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Akorinto 13:13 - Buku Lopatulika

Oyera mtima onse akupatsani moni.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Oyera mtima onse akupatsani moni.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Anthu onse a Mulungu akukupatsani moni.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Anthu onse a Mulungu akupereka moni.

Onani mutuwo



2 Akorinto 13:13
9 Mawu Ofanana  

Ndipo ngati mupatsa moni abale anu okhaokha, muchitanji choposa ena? Kodi angakhale anthu akunja sachita chomwecho?


Mupatsane moni wina ndi mnzake ndi kupsompsonana kopatulika. Mipingo yonse ya Khristu ikupatsani moni.


Perekani moni kwa atsogoleri anu onse, ndi oyera mtima onse. Akupatsani moni iwo a ku Italiya.


Iye wa ku Babiloni wosankhidwa pamodzi nanu akukupatsani moni; ateronso Marko mwana wanga.


Akupereka moni ana a mbale wanu wosankhika.


koma ndiyembekeza kukuona iwe msanga, ndipo tidzalankhula popenyana.