Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Akorinto 12:8 - Buku Lopatulika

Za ichi ndinapemphera Ambuye katatu kuti chichoke kwa ine.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Za ichi ndinapemphera Ambuye katatu kuti chichoke kwa ine.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Pamenepo ndidapempha Ambuye katatu kuti andichotsere chimenechi,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Katatu konse ndinapempha Ambuye kuti andichotsere.

Onani mutuwo



2 Akorinto 12:8
10 Mawu Ofanana  

Ndipo ukatsuka chovalacho, kapena muyaro, kapena mtsendero, kapena chinthu chilichonse chopangika ndi chikopa, ngati nthenda yalekapo pa chimenecho, achitsukenso kawiri, pamenepo chili choyera.


Ndipo ichi chinachitika katatu; ndipo zinakwezekanso zonse kumwamba.


Ndipo momwemonso Mzimu athandiza kufooka kwathu; pakuti chimene tizipempha monga chiyenera, sitidziwa; koma Mzimu mwini atipempherera ndi zobuula zosatheka kuneneka;


Ameneyo, m'masiku a thupi lake anapereka mapemphero ndi mapembedzero pamodzi ndi kulira kwakukulu ndi misozi kwa Iye amene anakhoza kumpulumutsa Iye muimfa, ndipo anamveka popeza anaopa Mulungu,


Kundichititsa chisoni kuti ndinaika Saulo akhale mfumu; pakuti wabwerera wosanditsata Ine, ndipo sanachite malamulo anga. Ndipo Samuele anakwiya; nalira kwa Yehova usiku wonse.