Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Akorinto 11:5 - Buku Lopatulika

Pakuti ndiyesa kuti sindinaperewere konse ndi atumwi oposatu.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti ndiyesa kuti sindinaperewera konse ndi atumwi oposatu.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ndikuganiza kuti atumwi anu apamwambawo sandiposa ine pa kanthu kalikonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Komatu sindikuganiza kuti ndine wotsika kwambiri kwa “atumwi apamwamba.”

Onani mutuwo



2 Akorinto 11:5
3 Mawu Ofanana  

Koma ndi chisomo cha Mulungu ndili ine amene ndili; ndipo chisomo chake cha kwa ine sichinakhale chopanda pake, koma ndinagwirira ntchito yochuluka ya iwo onse; koma si ine, koma chisomo cha Mulungu chakukhala ndi ine.