Koma ndi chisomo cha Mulungu ndili ine amene ndili; ndipo chisomo chake cha kwa ine sichinakhale chopanda pake, koma ndinagwirira ntchito yochuluka ya iwo onse; koma si ine, koma chisomo cha Mulungu chakukhala ndi ine.
2 Akorinto 11:5 - Buku Lopatulika Pakuti ndiyesa kuti sindinaperewere konse ndi atumwi oposatu. Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014 Pakuti ndiyesa kuti sindinaperewera konse ndi atumwi oposatu. Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa Ndikuganiza kuti atumwi anu apamwambawo sandiposa ine pa kanthu kalikonse. Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero Komatu sindikuganiza kuti ndine wotsika kwambiri kwa “atumwi apamwamba.” |
Koma ndi chisomo cha Mulungu ndili ine amene ndili; ndipo chisomo chake cha kwa ine sichinakhale chopanda pake, koma ndinagwirira ntchito yochuluka ya iwo onse; koma si ine, koma chisomo cha Mulungu chakukhala ndi ine.