Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Akorinto 11:30 - Buku Lopatulika

Ngati ndiyenera kudzitamandira, ndidzadzitamandira ndi za kufooka kwanga.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ngati ndiyenera kudzitamandira, ndidzadzitamandira ndi za kufooka kwanga.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ngati ndiyenera kunyada, ndidzanyadira kufooka kwanga.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ngati nʼkoyenera kudzitamandira, ndidzadzitamandira pa zinthu zimene zimaonetsa kufowoka kwanga.

Onani mutuwo



2 Akorinto 11:30
9 Mawu Ofanana  

Kudya uchi wambiri sikuli kwabwino; chomwecho kufunafuna ulemu wakowako sikuli ulemu.


Wina akutume, si m'kamwa mwako ai; mlendo, si milomo ya iwe wekha.


Ndipo Yesu anayendayenda mu Galileya monse, analikuphunzitsa m'masunagoge mwao, nalalikira Uthenga Wabwino wa Ufumu, nachiritsa nthenda zonse ndi kudwala konse mwa anthu.


Ndipo ine ndinakhala nanu mofooka ndi m'mantha, ndi monthunthumira mwambiri.


Ndiyenera kudzitamandira, kungakhale sikupindulika; koma ndidzadza kumasomphenya ndi mavumbulutso a Ambuye.


Tsopano ndikondwera nazo zowawazo chifukwa cha inu, ndipo ndikwaniritsa zoperewera za chisautso cha Khristu m'thupi langa chifukwa cha thupi lake, ndilo Mpingowo;