Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Akorinto 11:24 - Buku Lopatulika

Kwa Ayuda ndinalandira kasanu mikwingwirima makumi anai kuperewera umodzi.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Kwa Ayuda ndinalandira kasanu mikwingwirima makumi anai kuperewera umodzi.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kasanu Ayuda adandikwapula mikwapulo 39.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Andikwapulapo kasanu zikoti zija za Ayuda, makumi anayi kuchotsapo chimodzi.

Onani mutuwo



2 Akorinto 11:24
4 Mawu Ofanana  

Koma chenjerani ndi anthu; pakuti adzakuperekani inu ku bwalo la akulu a milandu, nadzakukwapulani inu m'masunagoge mwao;


Koma inu mudziyang'anire inu nokha; pakuti adzakuperekani inu ku bwalo la akulu a milandu; ndipo adzakukwapulani m'masunagoge; ndipo pamaso pa akazembe ndi mafumu mudzaimirira chifukwa cha Ine, kukhale umboni kwa iwo.


Ndipo kapolo uyo, wodziwa chifuniro cha mbuye wake, ndipo sanakonze, ndi kusachita zonga za chifuniro chakecho, adzakwapulidwa mikwapulo yambiri.