Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Akorinto 11:19 - Buku Lopatulika

Pakuti mulolana nao opanda nzeru mokondwera, pokhala anzeru inu nokha.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pakuti mulolana nao opanda nzeru mokondwera, pokhala anzeru inu nokha.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Inu mumati ndinu anzeru kwambiri, nchifukwa chake anthu opusa mumangoŵalekerera mokondwa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Inu mumalolera kukhala ndi zitsiru mokondwera chifukwa mumati ndinu anzeru!

Onani mutuwo



2 Akorinto 11:19
5 Mawu Ofanana  

Ndinena monga kwa anzeru; lingirirani inu chimene ndinena.


Tili opusa ife chifukwa cha Khristu, koma muli ochenjera inu mwa Khristu; tili ife ofooka, koma inu amphamvu; inu ndinu olemekezeka, koma ife ndife onyozeka.


Koma za zoperekedwa nsembe kwa mafano: Tidziwa kuti tili nacho chidziwitso tonse. Chidziwitso chitukumula, koma chikondi chimangirira.


Ndidziwa ntchito zako, ndi chilemetso chako ndi chipiriro chako ndi kuti sungathe kulola oipa, ndipo unayesa iwo amene adzitcha okha atumwi, osakhala atumwi, nuwapeza onama;


Chifukwa unena kuti ine ndine wolemera, ndipo chuma ndili nacho, osasowa kanthu; ndipo sudziwa kuti ndiwe watsoka, ndi wochititsa chifundo, ndi wosauka, ndi wakhungu, ndi wausiwa;