Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




2 Akorinto 10:17 - Buku Lopatulika

Koma iye wodzitamandira adzitamandire mwa Ambuye;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma iye wodzitamandira adzitamandire mwa Ambuye;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Paja Malembo akuti, “Wofuna kunyada, anyadire Ambuye.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Koma, “Ngati munthu akufuna kunyadira, anyadire mwa Ambuye.”

Onani mutuwo



2 Akorinto 10:17
13 Mawu Ofanana  

Mudzitamandire ndi dzina lake loyera: mitima yao ya iwo ofunsira Yehova ikondwere.


Kuti ndione chokomacho cha osankhika anu, kuti ndikondwere nacho chikondwerero cha anthu anu, kuti ndidzitamandire pamodzi ndi cholowa chanu.


Iwe udzawapeta, ndi mphepo idzawauluza; ndipo kamvulumvulu adzawamwaza; ndipo iwe udzasangalala mwa Yehova, udzadzikuza mwa Woyera wa Israele.


Mwa Yehova mbeu yonse ya Israele idzalungamitsidwa ndi kudzikuza.


chomwecho iye amene adzidalitsa yekha m'dziko lapansi, adzadzidalitsa yekha mwa Mulungu woona; ndipo iye amene alumbira m'dziko lapansi adzalumbira pa Mulungu woona; popeza zovuta zoyamba zaiwalika, ndi popeza zabisalika kumaso kwanga.


Ndipo udzalumbira, Pali Yehova m'zoonadi, m'chiweruziro, ndi m'chilungamo; ndipo mitundu ya anthu idzadzidalitsa mwa Iye, ndipo mwa Iye adzatamandira.


Ndipo si chotero chokha, koma ife tikondwera ndi Mulungu mwa Ambuye wathu Yesu Khristu, amene talandira naye tsopano chiyanjanitso.


kuti thupi lililonse lisadzitamande pamaso pa Mulungu.


kuti monga mwalembedwa, Iye amene adzitamanda, adzitamande mwa Ambuye.


pakuti ife ndife mdulidwe, akutumikira popembedza ndi Mzimu wa Mulungu, nadzitamandira mwa Khristu Yesu, osakhulupirira m'thupi;