Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Yohane 5:2 - Buku Lopatulika

Umo tizindikira kuti tikonda ana a Mulungu, pamene tikonda Mulungu, ndi kuchita malamulo ake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Umo tizindikira kuti tikonda ana a Mulungu, pamene tikonda Mulungu, ndi kuchita malamulo ake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Chodziŵira kuti timakonda ana a Mulungu nchakuti timakonda Mulungu ndi kutsata malamulo ake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Chodziwira kuti timakonda ana a Mulungu nʼchakuti timakonda Mulungu ndi kusunga malamulo ake.

Onani mutuwo



1 Yohane 5:2
7 Mawu Ofanana  

Zinthu izi ndilamula inu, kuti mukondane wina ndi mnzake.


Ndipo umo tizindikira kuti tamzindikira Iye, ngati tisunga malamulo ake.


koma iye amene akasunga mau ake, mwa iyeyu zedi chikondi cha Mulungu chathedwa. M'menemo tizindikira kuti tili mwa Iye;


Ife tidziwa kuti tachokera kutuluka muimfa kulowa m'moyo, chifukwa tikondana ndi abale. Iye amene sakonda akhala muimfa.


Ndipo lamulo ili tili nalo lochokera kwa Iye, kuti iye amene akonda Mulungu akondenso mbale wake.