Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Timoteyo 1:8 - Buku Lopatulika

Koma mudziwa kuti lamulo ndi labwino, ngati munthu achita nalo monga mwa lamulo,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma mudziwa kuti lamulo ndi labwino, ngati munthu achita nalo monga mwa lamulo,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tikudziŵa kuti Malamulo ngabwino, malinga nkuŵagwiritsa ntchito moyenera.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Tikudziwa kuti Malamulo ndi abwino ngati munthu awagwiritsa ntchito bwino.

Onani mutuwo



1 Timoteyo 1:8
12 Mawu Ofanana  

Munatsikiranso paphiri la Sinai, nimunalankhula nao mochokera mu Mwamba, ndipo munawapatsa maweruzo oyenera, ndi chilamulo choona, malemba, ndi malamulo okoma;


Ndipo musafanizidwe ndi makhalidwe a pansi pano: koma mukhale osandulika, mwa kukonzanso kwa mtima wanu, kuti mukazindikire chimene chili chifuniro cha Mulungu, chabwino, ndi chokondweretsa, ndi changwiro.


Koma ngati ndichita chimene sindichifuna, ndivomerezana nacho chilamulo kuti chili chabwino.


Pakuti ndidziwa kuti m'kati mwanga, ndiko m'thupi langa, simukhala chinthu chabwino; pakuti kufuna ndili nako, koma kuchita chabwino sindikupeza.


Pakuti monga mwa munthu wa m'kati mwanga, ine ndikondwera ndi chilamulo cha Mulungu:


Pamenepo kodi chilamulo chitsutsana nao malonjezano a Mulungu? Msatero ai. Pakuti chikadapatsidwa chilamulo chakukhoza kuchitira moyo, chilungamo chikadachokera ndithu kulamulo.


Koma ngatinso wina ayesana nao m'makani amasewero, samveka korona ngati sanayesane monga adapangana.