Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 7:15 - Buku Lopatulika

ndipo Samuele anaweruza Israele masiku onse a moyo wake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndipo Samuele anaweruza Israele masiku onse a moyo wake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Samuele adatsogolera Aisraele moyo wake wonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Samueli anatsogolera Aisraeli moyo wake wonse.

Onani mutuwo



1 Samueli 7:15
8 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anautsa oweruza, amene anawapulumutsa m'dzanja la iwo akuwafunkha.


Ndipo Samuele anauza Aisraele onse, kuti, Onani ndinamvera mau anu mwa zonse munalankhula ndi ine, ndipo ndinakulongerani mfumu.


Ndipo Yehova anatumiza Yerubaala, ndi Baraki, ndi Yefita, ndi Samuele, napulumutsa inu m'manja mwa adani anu pozungulira ponse, ndipo munakhala mosatekeseka.


Ndipo Samuele anamwalira; ndi Aisraele onse anaunjikana pamodzi nalira maliro ake, namuika m'nyumba yake ku Rama. Davide ananyamuka, natsikira ku chipululu cha Parani.


Ndipo anayenda chozungulira chaka ndi chaka ku Betele, ndi ku Giligala, ndi ku Mizipa; naweruza Israele m'malo onse amenewa.


Ndipo anaunjikana ku Mizipa, natunga madzi, nawatsanula pamaso pa Yehova, nasala chakudya tsiku lija, nati, Tinachimwira Yehova. Ndipo Samuele anaweruza ana a Israele mu Mizipa.