Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 31:11 - Buku Lopatulika

Koma pamene a ku Yabesi-Giliyadi anamva zimene Afilisti anamchitira Saulo,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Koma pamene a ku Yabesi-Giliyadi anamva zimene Afilisti anamchitira Saulo,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Koma anthu a ku Yabesi-Giliyadi atamva zimene Afilisti adaamchita Saulo,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pamene anthu a ku Yabesi Giliyadi anamva zimene Afilisti anachitira Sauli,

Onani mutuwo



1 Samueli 31:11
5 Mawu Ofanana  

Ndipo anthu Ayuda anabwera namdzoza Davide pomwepo akhale mfumu ya nyumba ya Yuda. Ndipo wina anauza Davide kuti, Anthu a ku Yabesi-Giliyadi ndiwo amene anamuika Saulo.


Ndipo Davide ananka natenga mafupa a Saulo ndi mafupa a Yonatani mwana wake kwa anthu a ku Yabesi-Giliyadi amene anawaba m'khwalala la Beteseani, kumene Afilisti adawapachika, tsiku lija Afilistiwo anapha Saulo ku Gilibowa;


Ndipo onse a Yabesi-Giliyadi, atamva zonse Afilisti adachitira Saulo,


Nati iwo, Kodi pali lina la mafuko a Israele losakwera kudza kwa Yehova ku Mizipa? Ndipo taonani, kuchokera ku Yabesi-Giliyadi sanadze mmodzi kumisasa, kumsonkhano.