Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 30:30 - Buku Lopatulika

ndi kwa iwo a ku Horoma, ndi kwa iwo a ku Borasani, ndi kwa iwo a ku Ataki;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

ndi kwa iwo a ku Horoma, ndi kwa iwo a ku Borasani, ndi kwa iwo a ku Ataki;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

a ku Horoma, a ku Borasani, a ku Ataki

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

a ku Horima, Borasani, Ataki,

Onani mutuwo



1 Samueli 30:30
8 Mawu Ofanana  

Pamenepo anatsika Aamaleke, ndi Akanani, akukhala m'phirimo nawakantha, nawapha kufikira ku Horoma.


Ndipo Yehova anamvera mau a Israele, napereka Akanani; ndipo anawaononga konse ndi mizinda yao yomwe; natcha dzina lake la malowo Horoma.


mfumu ya ku Horoma, imodzi; mfumu ya ku Aradi, imodzi;


ndi Elitoladi, ndi Kesili ndi Horoma;


Libina ndi Eteri ndi Asani;


ndi Elitoladi, ndi Betuli, ndi Horoma;


Aini, Rimoni ndi Eteri ndi Asani; mizinda inai ndi midzi yao;


Ndipo Yuda anamuka ndi Simeoni mkulu wake, nakantha Akanani akukhala mu Zefati, nauononga konse. Koma dzina la mzindawo analitcha Horoma.