Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 30:18 - Buku Lopatulika

Ndipo Davide analanditsa zonse anazitenga Aamaleke, napulumutsa akazi ake awiri.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Davide analanditsa zonse anazitenga Aamaleke, napulumutsa akazi ake awiri.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Motero Davide adalanditsa zinthu zonse zimene adaatenga Aamaleke. Ndipo adapulumutsanso akazi ake aŵiri aja.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Choncho Davide analanditsa zinthu zonse zimene Aamaleki aja anatenga. Anapulumutsanso akazi ake awiri aja.

Onani mutuwo



1 Samueli 30:18
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anabwera nacho chuma chonse, nabwera naye Loti yemwe ndi chuma chake, ndi akazi ndi anthu omwe.


anatenga anthu onse, nanka kukamenyena ndi Ismaele mwana wa Netaniya, nampeza pamadzi ambiri a mu Gibiyoni.


nati kwa Mose, Atumiki anu anawerenga ankhondo tinali nao, ndipo sanasowe munthu mmodzi wa ife.


Ndipo Davide anafunsira kwa Yehova, nati, Ndikalondola khamulo ndidzalipeza kodi? Ndipo anamyankha kuti, Londola, pakuti zoonadi udzawapeza, ndi kulanditsa zonse.