1 Samueli 27:12 - Buku Lopatulika
Ndipo Akisi anakhulupirira Davide, nati, Anadziipitsa ndithu pakati pa anthu a Israele, chifukwa chake iye adzakhala mnyamata wanga chikhalire.
Onani mutuwo
Ndipo Akisi anakhulupirira Davide, nati, Anadziipitsa ndithu pakati pa anthu a Israele, chifukwa chake iye adzakhala mnyamata wanga chikhalire.
Onani mutuwo
Ndipo Akisi adamkhulupirira Davide namaganiza kuti, “Davide wadzisandutsa munthu woipa wodedwa ndi anthu ake omwe Aisraele. Nchifukwa chake adzakhala mtumiki wanga pa moyo wake wonse.”
Onani mutuwo
Akisi ankamukhulupirira Davide ndipo ankati mu mtima mwake, “Davide wadzisandutsa munthu woyipa kwambiri pakati pa anthu ake omwe, Aisraeli. Tsono adzakhala mtumiki wanga mpaka kalekale.”
Onani mutuwo