Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 25:4 - Buku Lopatulika

Ndipo Davide anamva kuchipululu kuti Nabala alinkusenga nkhosa zake.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Davide anamva kuchipululu kuti Nabala alinkusenga nkhosa zake.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Davide anali atamva kuchipululu kuja kuti Nabala akumeta nkhosa zake.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Davide anamva akanali ku chipululu kuti Nabala akumeta nkhosa.

Onani mutuwo



1 Samueli 25:4
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anamuuza Tamara, kuti, Taona, mpongozi wako akwera kunka ku Timna kuti akasenge nkhosa zake.


Ndipo zitapita zaka ziwiri zathunthu, kunali kuti Abisalomu anali nao osenga nkhosa zake ku Baala-Hazori pafupi pa Efuremu; ndipo Abisalomu anaitana ana aamuna onse a mfumu.


Tsono dzina la munthuyo ndiye Nabala, ndi dzina la mkazi wake ndiye Abigaile; ndiye mkazi wa nzeru yabwino, ndi wa nkhope yokongola; koma mwamunayo anali waphunzo ndi woipa machitidwe ake; ndipo iye anali wa banja la Kalebe.


Davide natuma anyamata khumi, nanena kwa anyamatawo, Mukwere ku Karimele, mumuke kwa Nabala ndi kundiperekera moni;