1 Samueli 23:26 - Buku Lopatulika
Ndipo Saulo anamuka mbali ina ya phiri, Davide ndi anthu ake kuseri kwake; ndipo Davide anafulumira kuthawa, chifukwa cha kuopa Saulo; popeza Saulo ndi anthu ake anazinga Davide ndi anthu ake kwete kuti awagwire.
Onani mutuwo
Ndipo Saulo anamuka mbali ina ya phiri, Davide ndi anthu ake kuseri kwake; ndipo Davide anafulumira kuthawa, chifukwa cha kuopa Saulo; popeza Saulo ndi anthu ake anazinga Davide ndi anthu ake kwete kuti awagwire.
Onani mutuwo
Saulo adadzera mbali ina ya phiri, Davide ndi anthu ake adadzeranso mbali ina ya phirilo. Tsono Davide ndi anthu ake adafulumira kuthaŵa, pamene Saulo ndi anthu ake anali pafupi kuŵagwira.
Onani mutuwo
Sauli amayenda mbali ina ya phirilo, ndipo Davide ndi anthu ake nawonso anali mbali ina ya phirilo. Koma Davide ndi anthu ake anafulumira kumuthawa Sauli pamene Sauliyo ndi anthu ake ali pafupi kuwagwira.
Onani mutuwo