Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 19:6 - Buku Lopatulika

Ndipo Saulo anamvera mau a Yonatani; nalumbira, Pali Yehova, sadzaphedwa iye.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Saulo anamvera mau a Yonatani; nalumbira, Pali Yehova, sadzaphedwa iye.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Saulo adamvera mau a Yonatani, ndipo adalumbira kuti, “Mulungudi! Davideyo sadzaphedwa!”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Sauli anamvera mawu a Yonatani ndipo analumbira kuti, “Pali Yehova, Davide sadzaphedwa.”

Onani mutuwo



1 Samueli 19:6
9 Mawu Ofanana  

M'maso mwake munthu woonongeka anyozeka; koma awachitira ulemu akuopa Yehova. Atalumbira kwa tsoka lake, sasintha ai.


Tsegula pakamwa pako, ukanenere wosalankhula, ndi mlandu wa amasiye onse.


Ndipo ngakhale ati, Pali Yehova; komatu alumbira monama.


Pakuti, pali Yehova wakupulumutsa Israele, chingakhale chili m'mwana wanga Yonatani, koma adzafa ndithu. Koma pakati pa anthu onse panalibe mmodzi wakumyankha iye.


popeza iye anataya moyo wake nakantha Mfilistiyo, ndipo Yehova anachitira Aisraele onse chipulumutso chachikulu, inu munachiona, nimunakondwera; tsono mudzachimwiranji mwazi wosalakwa, ndi kumupha Davide popanda chifukwa?


Pamenepo Yonatani anaitana Davide, namuuza zonsezi. Ndipo Yonatani anafika naye Davide kwa Saulo, iye nakhalanso pamaso pake monga kale.


Ndipo Saulo anamlumbirira kwa Yehova, nati, Pali Yehova, palibe chilango chidzakugwera chifukwa cha chinthu ichi.