Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 19:22 - Buku Lopatulika

Pamenepo iyenso anamuka ku Rama, nafika ku chitsime chachikulu chili ku Seku, nafunsa nati, Samuele ndi Davide ali kuti? Ndipo wina anati, Taonani, ali ku Nayoti mu Rama.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo iyenso anamuka ku Rama, nafika ku chitsime chachikulu chili ku Seku, nafunsa nati, Samuele ndi Davide ali kuti? Ndipo wina anati, Taonani, ali ku Nayoti m'Rama.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Choncho Saulo mwini wake adanyamuka napita ku Rama, nakafika pa chitsime chachikulu chimene chili ku Seku. Ndipo adafunsa kuti, “Kodi Samuele ndi Davide ali kuti?” Munthu wina adati, “Ali ku Nayoti ku Rama.”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Pomaliza Sauli mwini wake ananyamuka kupita ku Rama ndipo anafika ku chitsime chachikulu cha ku Seku. Ndipo anafunsa, “Samueli ndi Davide ali kuti?” Munthu wina anamuyankha kuti, “Ali ku Nayoti ku Rama.”

Onani mutuwo



1 Samueli 19:22
3 Mawu Ofanana  

Chomwecho anathawa Davide, napulumuka, nafika kwa Samuele ku Rama, namuuza zonse Saulo anamchitira. Ndipo iye ndi Samuele anakhala ku Nayoti.


Ndipo pamene anauza Saulo, iye anatumiza mithenga ina; koma iyonso inanenera. Ndipo Saulo anatumiza mithenga kachitatu, nayonso inanenera.


Ndipo anapita komweko ku Nayoti mu Rama; ndi mzimu wa Mulungu unamgwera iyenso; ndipo anapitirira, nanenera, mpaka anafika ku Nayoti mu Rama.