Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 19:19 - Buku Lopatulika

Ndipo wina anauza Saulo, kuti, Onani Davide ali ku Nayoti mu Rama.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo wina anauza Saulo, kuti, Onani Davide ali ku Nayoti m'Rama.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Saulo atamva kuti Davide ali ku Nayoti ku Rama,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Sauli anamva kuti, “Davide ali ku Nayoti ku Rama.”

Onani mutuwo



1 Samueli 19:19
6 Mawu Ofanana  

Mkulu akamvera chinyengo, atumiki ake onse ali oipa.


Chomwecho anathawa Davide, napulumuka, nafika kwa Samuele ku Rama, namuuza zonse Saulo anamchitira. Ndipo iye ndi Samuele anakhala ku Nayoti.


Ndipo Saulo anatumiza mithenga kuti igwire Davide, ndipo pamene inaona gulu la aneneri alikunenera, ndi Samuele mkulu wao alikuimapo, mzimu wa Mulungu unagwera mithenga ya Saulo, ninenera iyonso.


Ndipo a ku Zifi anakwera kwa Saulo ku Gibea, nati, Davide salikubisala kwathu kodi, m'ngaka za m'nkhalango ku Horesi, m'phiri la Hakila, limene lili kumwera kwa chipululu?


Ndipo Azifi anafika kwa Saulo ku Gibea, nati, Kodi Davide sali kubisala m'phiri la Hakila, kupenya kuchipululu!