Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 18:29 - Buku Lopatulika

Saulo nayamba kumuopa Davide kopambana; ndi Saulo anali mdani wa Davide masiku onse.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Saulo nayamba kumuopa Davide kopambana; ndi Saulo anali mdani wa Davide masiku onse.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

adamuwopabe kwambiri ndi kudana naye moyo wake wonse.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

iye anapitirirabe kumuopa Davide ndi kumadana naye moyo wake wonse.

Onani mutuwo



1 Samueli 18:29
10 Mawu Ofanana  

Ndiponso ndinapenyera mavuto onse ndi ntchito zonse zompindulira bwino, kuti chifukwa cha zimenezi anansi ake achitira munthu nsanje. Ichinso ndi chabe ndi kungosautsa mtima.


Chifukwa chake, kuyambira tsiku lomwelo anapangana kuti amuphe Iye.


Ukhulupirira iwe kuti Mulungu ali mmodzi; uchita bwino; ziwanda zikhulupiriranso, ndipo zinthunthumira.


Ndipo Saulo anaopa Davide chifukwa Yehova anali naye, koma adamchokera Saulo.


Ndipo pamene Saulo anaona kuti analikukhala wochenjera ndithu anamuopa.


Ndipo Saulo anaona, nadziwa kuti Yehova ali ndi Davide; ndi kuti Mikala mwana wa Saulo anamkonda Davide.


Pomwepo mafumu a Afilisti anatuluka; ndipo nthawi zonse anatuluka iwo, Davide anali wochenjera koposa anyamata onse a Saulo, chomwecho dzina lake linatamidwa kwambiri.