Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 18:24 - Buku Lopatulika

Ndipo anyamata a Saulo anamuuza, kuti, Anatero Davide.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo anyamata a Saulo anamuuza, kuti, Anatero Davide.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Nduna za Saulo zidamuuza zonse zimene Davide adaanena.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Nduna za Sauli zinamuwuza zonse zimene anayankha Davide.

Onani mutuwo



1 Samueli 18:24
2 Mawu Ofanana  

Ndipo anyamata a Saulo analankhula mau awa m'makutu a Davide. Nati Davide, Kodi muchiyesera chinthu chopepuka kukhala mkamwini wa mfumu, popeza ndili munthu wosauka, ndi wopeputsidwa.


Nati Saulo, Mudzatero kwa Davide, kuti mfumu safuna cholowolera china, koma nsonga za makungu zana limodzi za Afilisti, kuti abwezere chilango adani a mfumu. Koma Saulo anaganizira kupha Davide ndi dzanja la Afilisti.