Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 18:15 - Buku Lopatulika

Ndipo pamene Saulo anaona kuti analikukhala wochenjera ndithu anamuopa.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo pamene Saulo anaona kuti analikukhala wochenjera ndithu anamuopa.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono pamene Saulo adaona kuti Davide akupambana kwambiri, adayamba kuchita naye mantha.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Sauli ataona momwe Davide ankapambanira, iye anamuopa kwambiri.

Onani mutuwo



1 Samueli 18:15
8 Mawu Ofanana  

Wodala munthu wakuchitira chifundo, nakongoletsa; adzalimbika nao mlandu wake poweruzidwa.


Muyendere munzeru ndi iwo akunja, kuchita machawi nthawi ingatayike.


Koma wina wa inu ikamsowa nzeru, apemphe kwa Mulungu, amene apatsa kwa onse modzala manja, niwosatonza; ndipo adzampatsa iye.


Koma nzeru yochokera kumwamba iyamba kukhala yoyera, nikhalanso yamtendere, yaulere, yomvera bwino, yodzala chifundo ndi zipatso zabwino, yopanda tsankho, yosadzikometsera pamaso.


Ndipo Saulo anaopa Davide chifukwa Yehova anali naye, koma adamchokera Saulo.


Ndipo Davide anakhala wochenjera m'mayendedwe ake onse; ndipo Yehova anali naye.


Koma Aisraele onse ndi Ayuda onse anamkonda Davide pakuti anawatsogolera kutuluka ndi kulowa nao.