Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 17:56 - Buku Lopatulika

Ndipo mfumu inati, Ufunsire kuti mnyamatayo ndi mwana wa yani.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo mfumu inati, Ufunsire kuti mnyamatayo ndi mwana wa yani.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Apo mfumu idati, “Kafunse kuti kodi mnyamata ameneyu ndi mwana wa yani?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Mfumu inati, “Pita kafufuze kuti mnyamata ameneyu ndi mwana wa yani.”

Onani mutuwo



1 Samueli 17:56
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Saulo anati kwa Davide, Sukhoza iwe kukomana ndi Mfilisti uyu kukaponyana naye; pakuti iwe ndiwe mnyamata, koma iye anazolowera nkhondo kuyambira ubwana wake.


Ndipo pamene Saulo anaona Davide alikutulukira kwa Mfilistiyo, iye anati kwa Abinere, kazembe wa khamu la nkhondo, Abinere, mnyamata uyu ndi mwana wa yani? Nati Abinere, Pali moyo wanu, mfumu, ngati ndidziwa.


Ndipo pamene Davide anabwera, atapha Mfilistiyo, Abinere anamtenga, nafika naye pamaso pa Saulo, mutu wa Mfilistiyo uli m'dzanja lake.