Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 17:29 - Buku Lopatulika

Ndipo Davide anati, Ndachitanji tsopano? Palibe chifukwa kodi?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Davide anati, Ndachitanji tsopano? Palibe chifukwa kodi?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Davide adati, “Kodi ndachimwa chiyani? Ndiye kuti ndileke nkulankhula komwe?”

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Davide anati, “Kodi ndachita chiyani ine? Kodi ndisamayankhule?”

Onani mutuwo



1 Samueli 17:29
6 Mawu Ofanana  

Mayankhidwe ofatsa abweza mkwiyo; koma mau owawitsa aputa msunamo.


Koma iye amene ali wauzimu ayesa zonse, koma iye yekha sayesedwa ndi mmodzi yense.


osabwezera choipa ndi choipa, kapena chipongwe ndi chipongwe, koma penatu madalitso; pakuti kudzatsata ichi mwaitanidwa, kuti mukalandire dalitso.


Ndipo Eliabu mkulu wake anamumva iye alikulankhula ndi anthu; ndipo Eliyabu anapsa mtima ndi Davide, nati, Unatsikiranji kuno? Ndi nkhosa zija zowerengeka unazisiya ndi yani, m'chipululu muja? Ine ndidziwa kudzikuza kwako ndi kuipa kwa mtima wako; pakuti watsika kuti udzaone nkhondoyi.


Napotolokera iye kwa munthu wina, nalankhula mau omwewo; ndipo anthu anamyankhanso monga momwemo.