Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 17:14 - Buku Lopatulika

Ndipo Davide anali wotsiriza; ndi akulu atatuwo anamtsata Saulo.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Davide anali wotsiriza; ndi akulu atatuwo anamtsata Saulo.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Davide anali mzime. Ana akuluakulu atatuwo ndiwo anali ku nkhondo ndi Saulo.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Davide ndiye anali mzime. Ana aakulu atatuwo ndiwo anapita ku nkhondo ndi Sauli.

Onani mutuwo



1 Samueli 17:14
3 Mawu Ofanana  

Yehova ndipo anati kwa iye, Mitundu iwiri ili m'mimba mwako, magulu awiri a anthu adzatuluka m'mimba mwako; gulu lina lidzapambana mphamvu ndi linzake; wamkulu adzakhala kapolo wa wamng'ono.


Ndipo Samuele anati kwa Yese, Ana anu ndi omwewa kodi? Nati iye, Watsala wina, mng'ono wa onse, ndipo taonani, iye alikuweta nkhosa. Ndipo Samuele anati kwa Yese, Tumiza munthu akamtenge; pakuti ife sitidzakhala pansi kufikira iye atadza kuno.


Koma Davide akamuka kwa Saulo, nabwerera kudzadyetsa nkhosa za atate wake ku Betelehemu.