Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 15:10 - Buku Lopatulika

Pamenepo mau a Yehova anafika kwa Samuele, nati,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Pamenepo mau a Yehova anafika kwa Samuele, nati,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Chauta adauza Samuele kuti,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kenaka Yehova anawuza Samueli kuti,

Onani mutuwo



1 Samueli 15:10
3 Mawu Ofanana  

Zitapita izo, mau a Yehova anadza kwa Abramu m'masomphenya, kuti, Usaope, Abramu, Ine ndine chikopa chako ndi mphotho yako yaikulukulu.


Kundichititsa chisoni kuti ndinaika Saulo akhale mfumu; pakuti wabwerera wosanditsata Ine, ndipo sanachite malamulo anga. Ndipo Samuele anakwiya; nalira kwa Yehova usiku wonse.


Koma Saulo ndi anthu anamsunga wamoyo Agagi, ndi nkhosa zokometsetsa, ndi ng'ombe, ndi zonenepa zina, ndi anaankhosa, ndi zabwino zonse sadafune kuzitha psiti; koma zonse zoipa ndi zonyansa anaziononga konsekonse.