Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Samueli 10:17 - Buku Lopatulika

Ndipo Samuele anaitana anthu onse asonkhane kwa Yehova ku Mizipa;

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndipo Samuele anaitana anthu onse asonkhane kwa Yehova ku Mizipa;

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Tsono Samuele adaitana anthu ku msonkhano wachipembedzo ku Mizipa.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Samueli anayitana Aisraeli onse kuti asonkhane pamaso pa Yehova ku Mizipa.

Onani mutuwo



1 Samueli 10:17
6 Mawu Ofanana  

Ndinakupatsa mfumu mu mkwiyo wanga; ndinamchotsanso mu ukali wanga.


Pamenepo Yefita anamuka ndi akulu a Giliyadi, ndipo anthu anamuika mkulu wao ndi mtsogoleri wao; ndipo Yefita ananena mau ake onse pamaso pa Yehova ku Mizipa.


Pamenepo anatuluka ana onse a Israele, nuunjikana msonkhano kwa Yehova ku Mizipa ngati munthu mmodzi, kuyambira ku Dani mpaka Beereseba ndi dziko la Giliyadi lomwe.


Ndipo anthu onse anapita ku Giligala; ndi kumeneko analonga Saulo mfumu pamaso pa Yehova mu Giligala; ndi pamenepo anaphera nsembe zoyamika pamaso pa Yehova; ndi pomwepo Saulo ndi anthu onse a Israele anakondwera kwakukulu.


Ndipo anayenda chozungulira chaka ndi chaka ku Betele, ndi ku Giligala, ndi ku Mizipa; naweruza Israele m'malo onse amenewa.