Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Mbiri 2:9 - Buku Lopatulika

Ndi ana a Hezironi anambadwirawo: Yerameele, ndi Ramu, ndi Kalebe.

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Ndi ana a Hezironi anambadwirawo: Yerameele, ndi Ramu, ndi Kalebe.

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Ana amene adabereka Hezironi naŵa: Yerameele, Ramu ndi Kelebe.

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Ana amene anabadwa kwa Hezironi anali: Yerahimeeli, Ramu ndi Kelubai.

Onani mutuwo



1 Mbiri 2:9
10 Mawu Ofanana  

Ndi Ramu anabala Aminadabu; ndi Aminadabu anabala Nasoni kalonga wa ana a Yuda;


Ndipo atafa Hezironi mu Kalebe-Efurata, Abiya mkazi wa Hezironi anambalira Asiriya atate wa Tekowa.


Ndi ana a Yerameele mwana woyamba wa Hezironi ndiwo: woyamba Ramu, ndi Buna, ndi Oreni, ndi Ozemu, ndi Ahiya.


Ndi ana a Kalebe mbale wa Yerameele ndiwo Mesa mwana wake woyamba, ndiye atate wa Zifi; ndi ana a Maresa atate wa Hebroni.


Ndi mwana wa Etani: Azariya.


ndi Yuda anabala Perezi ndi Zera mwa Tamara; ndi Perezi anabala Hezironi; ndi Hezironi anabala Ramu;


Ndipo iye anadza kudziko lonse la m'mbali mwa Yordani, nalalikira ubatizo wa kulapa mtima kuloza ku chikhululukiro cha machimo;


ndi Hezironi anabala Ramu, ndi Ramu anabala Aminadabu;


Ndipo Akisi anati, Waponyana nkhondo ndi yani lero? Nati Davide, Ndi a kumwera kwa Ayuda, ndi a kumwera kwa Ayerameele, ndi a kumwera kwa Akeni.