Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Mbiri 1:3 - Buku Lopatulika

Enoki, Metusela, Lameki,

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Enoki, Metusela, Lameki,

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Yaredi adabereka Enoki, Enoki adabereka Metusela, Metusela adabereka Lameki,

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Enoki, Metusela, Lameki, Nowa.

Onani mutuwo



1 Mbiri 1:3
6 Mawu Ofanana  

Kenani, Mahalalele, Yaredi,


Nowa, Semu, Hamu, ndi Yafeti.


Ndi chikhulupiriro Enoki anatengedwa kuti angaone imfa; ndipo sanapezeke, popeza Mulungu adamtenga: pakuti asanamtenge, anachitidwa umboni kuti anakondweretsa Mulungu;


Ndipo kwa iwo, Enoki, wachisanu ndi chiwiri kuyambira kwa Adamu, ananenera kuti, Taona, wadza Ambuye ndi oyera ake zikwi makumi,