Baibulo la pa intaneti

Zotsatsa


Baibulo lonse Chipangano Chakale Chipangano Chatsopano




1 Akorinto 9:4 - Buku Lopatulika

Kodi tilibe ulamuliro wa kudya ndi kumwa?

Onani mutuwo

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

Kodi tilibe ulamuliro wa kudya ndi kumwa?

Onani mutuwo

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

Kodi si koyenerera kwa ife kumalandira chakudya ndi chakumwa?

Onani mutuwo

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

Kodi ife tilibe ulamuliro wakudya ndi kumwa?

Onani mutuwo



1 Akorinto 9:4
11 Mawu Ofanana  

Koma litalowa dzuwa, adzakhala woyera, ndi pambuyo pake adyeko zoyerazo, popeza ndizo chakudya chake.


kapena thumba la kamba la kunjira, kapena malaya awiri, kapena nsapato, kapena ndodo; pakuti wantchito ayenera kulandira zakudya zake.


Ndipo m'nyumba momwemo khalani, ndi kudya ndi kumwa za kwao; pakuti wantchito ayenera mphotho yake; musachokachoka m'nyumba.


Sindinasirira siliva, kapena golide, kapena chovala cha munthu aliyense.


Chodzikanira changa kwa iwo amene andifunsa ine ndi ichi:


Koma iye amene aphunzira mau, ayenera kuchereza womphunzitsayo m'zonse zabwino.


kapena sitinakhale ofuna ulemerero wa kwa anthu, kapena kwa inu, kapena kwa ena, tingakhale tinali nayo mphamvu yakukulemetsani monga atumwi a Khristu.


Pakuti mukumbukira, abale, chigwiritso chathu ndi chivuto chathu; pochita usiku ndi usana, kuti tingalemetse wina wa inu, tinalalikira kwa inu Uthenga Wabwino wa Mulungu.